Eksodo 23:11 BL92

11 koma caka cacisanu ndi ciwiri uuleke, ugone; kuti aumphawi a anthu a mtundu wako adyemo ndipo zotsalira iwowa zoweta za kubusa zizidye; momwemo uzicita ndi munda wako wamphesa, ndimundawakowaazitona.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 23

Onani Eksodo 23:11 nkhani