Eksodo 23:19 BL92

19 Uzibweca nazo zoyambayamba za m'munda mwako ku nyumba ya Yehova Mulungu wako. Usaphike mwana wa mbuzi mu mkaka wa mace.Mulungu aloniezana nao za Kanani.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 23

Onani Eksodo 23:19 nkhani