Eksodo 26:4 BL92

4 Ndipo uziika magango a nsaru yamadzi m'mphepete mwace mwa nsaru imodzi, ku mkawo wa cilumikizano; nucite momwemo m'mphepete mwace mwa nsaru ya kuthungoya cilumikizano dna.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 26

Onani Eksodo 26:4 nkhani