Eksodo 28:1 BL92

1 Ndipo akuyandikire Aroni mbale wako, ndi ana ace amuna pamodzi naye, mwa ana a Israyeli, kuti andicitire Ine nchito ya nsembe, ndiwo Aroni, Nadabu, ndi Abihu, Eleazara ndi ltamara, ana a Aroni.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 28

Onani Eksodo 28:1 nkhani