Eksodo 31:13 BL92

13 Koma iwe, lankhula ndi ana a Israyeli, ndi kuti, Muzisunga masabata anga ndithu; pakuti ndiwo cizindikilo pakati pa Ine ndi inu mwa mibadwo yanu; kuti mudziwe kuti Ine ndine Yehova wakukupatulani.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 31

Onani Eksodo 31:13 nkhani