Eksodo 35:24 BL92

24 Yense wakupereka copereka ca siliva ndi mkuwa, anabwera naco copereka ca Yehova; ndi yense amene kwao kunapezeka mtengo wasitimu wa ku macitidwe onse a nchitoyi, anabwera nao.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 35

Onani Eksodo 35:24 nkhani