Eksodo 9:22 BL92

22 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Tambasula dzanja lako kuthambo, kuti pakhale matalala pa dziko lonse la Aigupto, pa anthu ndi pa zoweta, ndi pa zitsamba zonse za kuthengo, m'dziko la Aigupto.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 9

Onani Eksodo 9:22 nkhani