30 Ndipo Farao anauka usiku, iyendi anyamata ace onse, ndi Aaigupto onse; ndipo kunali kulira kwakukulu m'Aigupto; pakuti panalibe nyumba yopanda wakufa m'mwemo.
Werengani mutu wathunthu Eksodo 12
Onani Eksodo 12:30 nkhani