Eksodo 26:2 BL92

2 Utali wace wa nsaru yophimba imodzi ndiwo mikono makumi awiri kudza isanu ndi itatu, ndi kupingasa kwa nsaru imodzi ndiko mikono inai; nsaru zonse zikhale za muyeso umodzi.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 26

Onani Eksodo 26:2 nkhani