Eksodo 27:16 BL92

16 Ndipo pa cipata ca bwalolo pakhale nsaru yotsekera ya mikono makumi awiri, ya lamadzi ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, nchito ya wopikula; nsici zace zikhale zinai, ndi makamwa ao anai.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 27

Onani Eksodo 27:16 nkhani