Eksodo 34:6 BL92

6 Ndipo Yehova anapita pamaso pace, napfuula, Yehova, Yehova, Mulungu wacifundo ndi wacisomo, wolekereza, ndi wa ukoma mtima wocuruka, ndi wacoonadi;

Werengani mutu wathunthu Eksodo 34

Onani Eksodo 34:6 nkhani