Eksodo 14:26 BL92

26 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Tambasulira dzanja lako kunyanja, kuti madziwo abwerere kudzamiza Aaigupto, magareta ao, ndi apakavalo ao.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 14

Onani Eksodo 14:26 nkhani