Eksodo 14:27 BL92

27 Ndipo Mose anatambasulira dzanja lace kunyanja, ndi nyanja inabwerera m'mayendedwe ace mbanda kuca; ndipo Aaigupto pothawa anakomana nayo; ndipo Yehova anakutumula Aaigupto m'kati mwa nyanja.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 14

Onani Eksodo 14:27 nkhani