Eksodo 36:11 BL92

11 Ndipo anaika magango ansaru yamadzi m'mphepete mwace mwa nsaru imodzi ku mkawo wa cilumikizano; nacita momwemo m'mphepete mwace mwa nsaru ya kuthungo, ya cilumikizano caciwiri.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 36

Onani Eksodo 36:11 nkhani