11 Wa Benjamini, Abidana mwana wa Gideoni.
12 Wa Dani, Ahiyezeri mwana wa Amisadai.
13 Wa Aseri, Pagiyeli mwana wa Okirani.
14 Wa Gadi, Eliyasafe mwana wa Deyueli.
15 Wa Nafitali, Ahira mwana wa Enani.
16 Iwo ndiwo oitanidwa a khamu, akalonga a mapfuko a makolo ao; ndiwo akuru a zikwizo za Israyeli.
17 Ndipo Mose ndi Aroni anatenga anthu awa, onenedwa maina ao;