Numeri 1:32 BL92

32 A ana a Yosefe, ndiwo a ana a Efraimu, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akuturukira kunkhondo;

Werengani mutu wathunthu Numeri 1

Onani Numeri 1:32 nkhani