Numeri 10:9 BL92

9 Ndipo pamene mupita kunkhondo m'dziko lanu kucita nkhondo pa mdani wakusautsa inu, mulize cokweza ndi malipenga; ndipo Yehova Mulungu wanu adzakumbukila inu, nadzakupulumutsani kwa adani anu.

Werengani mutu wathunthu Numeri 10

Onani Numeri 10:9 nkhani