Numeri 11:1 BL92

1 Ndipo anthu anaipa, namadandaula m'makutu a Yehova; ndipo pamene Yehova anamva anapsa mtima; ndi mota wa Yehova unayaka pakati pao, nunyeketsa ku cilekezero ca cigono.

Werengani mutu wathunthu Numeri 11

Onani Numeri 11:1 nkhani