9 Cokhaci musamapikisana naye Yehova, musamaopa anthu a m'dzikomo; pakuti ndiwo mkate wathu; mthunzi wao wawacokera, ndipo Yehova ali nafe; musamawaopa.
Werengani mutu wathunthu Numeri 14
Onani Numeri 14:9 nkhani