Numeri 21:24 BL92

24 Ndipo Israyeli anamkantha ndi lupanga lakuthwa, nalanda dziko lace likhale lao lao, kuyambira Arinoni kufikira Yaboki, kufikira ana ai Amoni; popeza malire a ana a Amoni ndiwo olimba.

Werengani mutu wathunthu Numeri 21

Onani Numeri 21:24 nkhani