Numeri 26:10 BL92

10 ndipo dziko linayasama pakamwa pace, ndi kuwameza pamodzi ndi Kora, pakufa msonkhano uja; muja mote unaononga amuna mazana awiri ndi makumi asanu, nakhala iwo cizindikilo.

Werengani mutu wathunthu Numeri 26

Onani Numeri 26:10 nkhani