Numeri 26:12 BL92

12 Ana amuna a Simeoni monga mwa mabanja ao ndiwo: Nemueli, ndiye kholo la banja la Anemueli; Yamini, ndiye kholo la banja la Ayamini; Yakini, ndiye kholo la banja la Ayakini;

Werengani mutu wathunthu Numeri 26

Onani Numeri 26:12 nkhani