Numeri 26:15 BL92

15 Ana amuna a Gadi monga mwa mabanja ao ndiwo: Zefoni, ndiye kholo la banja la Azefoni; Hagi, ndiye kholo la banja la Ahagi; Suni, ndiye kholo la banja la Asuni;

Werengani mutu wathunthu Numeri 26

Onani Numeri 26:15 nkhani