Numeri 26:2 BL92

2 Werenga khamu lonse la ana a Israyeli, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, monga mwa nyumba za makolo ao, onse akuturukira kunkhondo m'Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Numeri 26

Onani Numeri 26:2 nkhani