Numeri 28:13 BL92

13 ndi limodzi la magawo khumi la ufa wosalala wosanganiza ndi mafuta, ukhale nsembe yaufa, ndiwo wa mwana wa nkhosa yense; ndiyo nsembe yopsereza ya pfungo lokoma, nsembe yamoto ya. Yehova.

Werengani mutu wathunthu Numeri 28

Onani Numeri 28:13 nkhani