Numeri 28:26 BL92

26 Momwemonso tsiku la zipatso zoyamba, pobwera nayo nsembe ya ufa watsopano kwa Yehova, m'madyerero anu a masabata, muzikhala nako kusonkhana kopatulika; musamacita nchito ya masiku ena.

Werengani mutu wathunthu Numeri 28

Onani Numeri 28:26 nkhani