Numeri 3:13 BL92

13 Pakuti ana oyamba onse ndi anga; tsiku lija ndinakantha ana oyamba onse m'dziko la Aigupto ndinadzipatulira ana oyamba onse m'Israyeli, kuyambira munthu kufikira coweta; ndiwo anga; Ine ndine Yehova.

Werengani mutu wathunthu Numeri 3

Onani Numeri 3:13 nkhani