Numeri 33:2 BL92

2 Ndipo Mose analembera maturukidwe ao monga mwa maulendo ao, monga mwa mau a Yehova; ndipo maulendo ao ndi awa monga mwa maturukidwe ao.

Werengani mutu wathunthu Numeri 33

Onani Numeri 33:2 nkhani