26 Wa pfuko la ana a Isakara, kalonga Palitiyeli mwana wa Azana.
27 Wa pfuko la ana a Aseri, kalonga Ahihudi mwana wa Selomi.
28 Wa pfuko la ana a Nafitali, kalonga Pedaheli mwana wa Amihudi.
29 Iwo ndiwo amene Yehova analamulira agawire ana a Israyeli colowa cao m'dziko la Kanani.