37 Awa ndi owerengedwa a mabanja a Akohati, onse akutumikira m'cihema cokomanako, amene Mose ndi Aroni anawawerenga monga mwa mau a Yehova mwa dzanja la Mose.
Werengani mutu wathunthu Numeri 4
Onani Numeri 4:37 nkhani