Numeri 6:20 BL92

20 ndipo wansembe aziweyula nsembe yoweyula pamaso pa Yehova; ici ncopatulikira wansembe, pamodzi ndi nganga ya nsembe yoweyula, pamodzi ndi mwendo wa nsembe yokweza; ndipo atatero Mnaziri amwe vinyo.

Werengani mutu wathunthu Numeri 6

Onani Numeri 6:20 nkhani