Numeri 18:2 BL92

2 Ndiponso abale ako, pfuko la Alevi, pfuko la kholo lako, uwayandikizitse pamodzi ndi iwe, kuti aphatikane ndi iwe, ndi kukutumikira; koma iwe ndi ana ako pamodzi ndi iwe mukhale ku khomo la cihema ca mboni.

Werengani mutu wathunthu Numeri 18

Onani Numeri 18:2 nkhani