Numeri 18:24 BL92

24 Popeza ndapatsa Alevi limodzi la magawo khumi, la ana a Israyeli, limene apereka nsembe, yokweza kwa Yehova, likhale colowa cao; cifukwa cace ndanena nao, Asadzakhale naco colowa mwa ana a Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Numeri 18

Onani Numeri 18:24 nkhani