Numeri 18:23 BL92

23 Koma Alevi azicita nchito ya cihema cokomanako, iwo ndiwo azisenza mphulupulu yao; ndilo lemba losatha mwa mibadwo yanu; ndipo asakhale naco colowa pakati pa ana a Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Numeri 18

Onani Numeri 18:23 nkhani