Numeri 2:16 BL92

16 Owerengedwa onse a cigono ca Rubeni ndiwo zikwi makumi khumi mphambu makumi asanu ndi cimodzi kudza mazana anai mphambu makumi asanu, monga mwa makamu ao. Ndiwo azitsatana nao otsogolerawo.

Werengani mutu wathunthu Numeri 2

Onani Numeri 2:16 nkhani