Numeri 25:6 BL92

6 Ndipo, taonani, anadza wina wa ana a Israyeli, nabwera naye mkazi Mmidyani kudza naye kwa abale ace, pamaso pa Mose, ndi pamaso pa khamu lonse la ana a Israyeli, pakulira iwo pa khomo la cihema cokomanako.

Werengani mutu wathunthu Numeri 25

Onani Numeri 25:6 nkhani