Numeri 6:12 BL92

12 Ndipo awapatulire Yehova masiku a kusala kwace, nadze nayo nkhosa yamphongo ya caka cimodzi ikhale nsembe yoparamula; koma masiku adapitawa azikhala cabe, popeza anadetsa kusala kwace.

Werengani mutu wathunthu Numeri 6

Onani Numeri 6:12 nkhani