Genesis 1:21 BL92

21 Mulungu ndipo adalenga zinsomba zazikuru ndi zoyendayenda zamoyo zakucuruka m'madzi mwa mitundu yao, ndi mbalame zamapiko, yonse monga mwa mtundu wace: ndipo anaona Mulungu kuti kunali kwabwino.

Werengani mutu wathunthu Genesis 1

Onani Genesis 1:21 nkhani