Genesis 16:6 BL92

6 Koma Abramu anati kwa Sarai, Taona, mdzakazi wako ali m'dzanja lako, umcitire iye cimene cikukomera m'maso mwako. Ndipo Sarai anamsautsa iye, ndipo anathawa kumaso kwace.

Werengani mutu wathunthu Genesis 16

Onani Genesis 16:6 nkhani