Genesis 18:5 BL92

5 ndipo ndidzatenga cakudya pang'ono, nimutonthoze mitima yanu; mutatero mudzapitirira, cifukwa mwafika kwa kapolo wanu. Ndipo anati, Cita comweco monga momwe wanena.

Werengani mutu wathunthu Genesis 18

Onani Genesis 18:5 nkhani