Genesis 19:34 BL92

34 Ndipo panali m'mamawa, woyamba anati kwa wamng'ono, Taona, ndinagona ine ndi atate wanga usiku walero: timwetsenso iye usikunso: udzalowe nugone naye kuti tisunge mbeu za atate wathu.

Werengani mutu wathunthu Genesis 19

Onani Genesis 19:34 nkhani