Genesis 22:12 BL92

12 Ndipo mthenga anati, Usaike dzanja lako pa mwana, usamcitire iye kanthu; cifukwa tsopano ndidziwa kuti iwe umuopa Mulungu, pakuti sunandikanize ine mwana wako, mwana wako wayekha.

Werengani mutu wathunthu Genesis 22

Onani Genesis 22:12 nkhani