Genesis 23:8 BL92

8 Ndipo ananena nao, kuti, Ngati mukandibvomereza kuti ndiike wakufa wanga ndisamthirenso maso, mundimvere ine, mundinenere ine kwa Efroni mwana wace wa Zohari,

Werengani mutu wathunthu Genesis 23

Onani Genesis 23:8 nkhani