Genesis 24:65 BL92

65 Ndipo anati kwa mnyamata, Munthuyo ndani amene ayenda m'munda kukomana ndi ife? Mnyamatayo ndipo anati, Uyo ndi mbuyanga: cifukwa cace namwali anatenga cophimba cace nadziphimba.

Werengani mutu wathunthu Genesis 24

Onani Genesis 24:65 nkhani