Genesis 25:18 BL92

18 Ndipo anakhala iwo kuyambira ku Havila kufikira ku Suri, ndiko kum'mawa kwace kwa Aigupto, pakunka ku Asuri: ndipo iye anakhala pamaso pa abale ace onse.

Werengani mutu wathunthu Genesis 25

Onani Genesis 25:18 nkhani