Genesis 28:14 BL92

14 mbeu zako zidzakhala monga pfumbi lapansi, ndipo udzabalalikira kumadzulo ndi kum'mawa ndi kumpoto ndi kumwera: mwa iwe ndi mu mbeu zako mabanja onse a dziko lapansi adzadalitsidwa.

Werengani mutu wathunthu Genesis 28

Onani Genesis 28:14 nkhani