Genesis 29:32 BL92

32 Ndipo Leyaanatenga pakati, nabala mwana wamwamuna, namucha dzina lace Rubeni; pakuti anati, Cifukwa kuti tsopano mwamuna wanga adzandikonda ine.

Werengani mutu wathunthu Genesis 29

Onani Genesis 29:32 nkhani