Genesis 30:14 BL92

14 Ndipo Rubeni ananka masiku akudula tirigu, napeza zipatso za mankhwala a cikondi m'thengo, nazitengera kwa amace Leva, Ndipo Rakele anati kwa Leya, Undipatseko mankhwala a mwana wako.

Werengani mutu wathunthu Genesis 30

Onani Genesis 30:14 nkhani