Genesis 30:16 BL92

16 Ndipo Yakobo anadza madzulo kucokera kumunda, ndipo Leya ananka kukomana naye, nati, Ulowe kwa ine cifukwa ndakulipilira iwe ndi mankhwala a mwana wanga. Ndipo anagona naye usiku womwewo.

Werengani mutu wathunthu Genesis 30

Onani Genesis 30:16 nkhani