Genesis 32:9 BL92

9 Ndipo Yakobo anati, Mulungu wa atate wanga Abrahamu, Mulungu wa atate wanga Isake, Yehova, amene munati kwa ine, Bwera ku dziko lako, ndi kwa abale ako, ndipo ndidzakucitira iwe bwino:

Werengani mutu wathunthu Genesis 32

Onani Genesis 32:9 nkhani